Pobwela pa nyumba panga uyenela ku nkala ndi ulemu
Cifukwa ngati ulibe ulemu nizakupanga Ngozi
Ine ndikonda antu a ulemu
Cifukwa ine niziba kucaya tu mambama twabwino
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu
Pobwela pa nyumba uyenela ku nkala ndi ulemu
Cifukwa bena sibafuna vo kambakamba
Vo kambakamba vi leta pamulomo
Cifukwa bena baziba kuyasha tukopo twa ngozi
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu
Peleka ulemu
Bena bacaya Ngozi yovuta
Kukopo
[?]
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu
Pobwela pa nyumba panga uyenela ku nkala ndi ulemu
Cifukwa, ine sinifuna vo kambakamba
Vo kambakamba vi leta pamulomo
Cifukwa bena baziba kuyasha tukopo twa ngozi
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu
Tiza cita cani
Kwa inu anzatu
Kuti mupeleke ulemu kwanzanu